Números 1

NYA vs NTLH

Sair da comparação
NTLH Nova Tradução na Linguagem de Hoje 2000
1 Yehova anayankhula ndi Mose mʼchipululu cha Sinai, mu tenti ya msonkhano, pa tsiku loyamba la mwezi wachiwiri, mʼchaka chachiwiri atatuluka mu Igupto, kuti,
1 No segundo ano depois da saída dos israelitas do Egito, no dia primeiro do segundo mês, o Senhor Deus falou com Moisés no deserto do Sinai, na Tenda Sagrada . Ele disse:
2 “Werengani Aisraeli onse mʼmafuko awo ndi mʼmabanja awo, lemba dzina la munthu wamwamuna aliyense, mmodzimmodzi.
2 — Você e Arão devem fazer a contagem do povo de Israel por grupos de famílias e por famílias.
3 Iwe ndi Aaroni mwawerenge mwa magulu awo mu Israeli, amuna onse a zaka makumi awiri zakubadwa ndi opitirirapo omwe angathe kugwira ntchito ya usilikali.
3 Façam a lista de todos os homens de vinte anos para cima, isto é, todos os que já têm idade para o serviço militar.
4 Munthu mmodzi wochokera ku fuko lililonse yemwe ndi mtsogoleri wa banja lake, ndiye akuthandizeni pa ntchitoyi.
4 Vocês chamarão um chefe de grupo de famílias de cada tribo para ajudá-los. São estes os nomes dos homens que vão ajudar vocês: Esses foram os chefes de tribo escolhidos no meio do povo de Israel para representar os seus grupos de famílias.
5 Mayina a anthu amene akuthandizeniwo ndi awa:
5 — ausente —
6 Selumieli mwana wa Zurisadai, kuchokera ku fuko la Simeoni,
6 — ausente —
7 Naasoni mwana wa Aminadabu, kuchokera ku fuko la Yuda,
7 — ausente —
8 Netanieli mwana wa Zuwara, kuchokera ku fuko la Isakara,
8 — ausente —
9 Eliabu mwana wa Heloni, kuchokera ku fuko la Zebuloni,
9 — ausente —
10 Mwa ana a Yosefe:
10 — ausente —
11 Abidani mwana wa Gideoni, kuchokera ku fuko la Benjamini,
11 — ausente —
12 Ahiyezeri mwana wa Amisadai, kuchokera ku fuko la Dani,
12 — ausente —
13 Pagieli mwana wa Okirani, kuchokera ku fuko la Aseri,
13 — ausente —
14 Eliyasafu mwana wa Deuweli, kuchokera ku fuko la Gadi,
14 — ausente —
15 Ahira mwana wa Enani, kuchokera ku fuko la Nafutali.”
15 — ausente —
16 Amenewa ndi anthu amene anasankhidwa kuchokera mʼmagulu mwawo, eni mbumba a mafuko a makolo awo. Iwowa anali atsogoleri a mafuko a Israeli.
16 — ausente —
17 Mose ndi Aaroni anatenga anthu amene mayina awo anaperekedwa,
17 — ausente —
18 ndipo pa tsiku loyamba la mwezi wachiwiri, anasonkhanitsa anthu onse pamodzi. Anthuwo anafotokoza za makolo awo mwa mafuko awo ndi mabanja awo. Ndipo mayina a amuna onse amene anali ndi zaka makumi awiri kapena kupitirirapo analembedwa, mmodzimmodzi
18 — ausente —
19 monga momwe Yehova analamulira Mose. Motero iyeyo anawawerenga mʼchipululu cha Sinai:
19 Assim, a contagem no deserto do Sinai foi feita como o Senhor havia ordenado a Moisés. Os homens de vinte anos para cima, que tinham idade para o serviço militar, foram registrados pelo seu nome, cada um no seu grupo de famílias e na sua família. Começaram pela tribo de Rúben, o filho mais velho de Jacó. A soma total das tribos foi a seguinte: Da tribo de Rúben, quarenta e seis mil e quinhentos homens.
20 Kuchokera mwa ana a Rubeni, mwana wamwamuna woyamba wa Israeli:
20 — ausente —
21 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Rubeni chinali 46,500.
21 — ausente —
22 Kuchokera mwa zidzukulu za Simeoni:
22 — ausente —
23 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Simeoni chinali 59,300.
23 — ausente —
24 Kuchokera mwa zidzukulu za Gadi:
24 — ausente —
25 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Gadi chinali 45, 650.
25 — ausente —
26 Kuchokera mwa zidzukulu za Yuda:
26 — ausente —
27 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Yuda chinali 74, 600.
27 — ausente —
28 Kuchokera mwa zidzukulu za Isakara:
28 — ausente —
29 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Isakara chinali 54,400.
29 — ausente —
30 Kuchokera mwa zidzukulu za Zebuloni:
30 — ausente —
31 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Zebuloni chinali 57,400.
31 — ausente —
32 Kuchokera mwa ana aamuna a Yosefe:
32 — ausente —
33 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Efereimu chinali 40,500.
33 — ausente —
34 Kuchokera mwa zidzukulu za Manase:
34 — ausente —
35 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Manase chinali 32,200.
35 — ausente —
36 Kuchokera mwa zidzukulu za Benjamini:
36 — ausente —
37 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Benjamini chinali 35,400.
37 — ausente —
38 Kuchokera mwa zidzukulu za Dani:
38 — ausente —
39 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Dani chinali 62,700.
39 — ausente —
40 Kuchokera mwa zidzukulu za Aseri:
40 — ausente —
41 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Aseri chinali 41,500.
41 — ausente —
42 Kuchokera mwa zidzukulu za Nafutali:
42 — ausente —
43 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Nafutali chinali 53,400.
43 — ausente —
44 Amenewa ndiwo anthu amene Mose ndi Aaroni anawawerenga mothandizidwa ndi atsogoleri khumi ndi awiri a Israeli, aliyense kuyimira fuko lake.
44 — ausente —
45 Aisraeli onse a zaka makumi awiri kapena kupitirirapo, omwe akanatha kugwira ntchito ya usilikali mʼgulu lankhondo la Israeli anawawerenga monga mwa mabanja awo.
45 — ausente —
46 Chiwerengero cha anthu onse pamodzi chinali 603,550.
46 — ausente —
47 Koma mabanja a fuko la Levi okha sanawawerenge pamodzi ndi ena.
47 Mas os levitas não foram registrados com as outras tribos ,
48 Pakuti Yehova anawuza Mose kuti,
48 pois o Senhor tinha dito a Moisés o seguinte:
49 “Usawerenge fuko la Levi kapena kuliphatikiza mʼkawundula wa Aisraeli.
49 — Quando você fizer a contagem dos homens com idade para o serviço militar, deixe de fora os homens da tribo de Levi.
50 Koma uyike Aleviwo kuti aziyangʼanira tenti yanga yopatulika, zipangizo zake ndi zonse zili mʼmenemo. Azinyamula tentiyo pamodzi ndi zipangizo zake zonse; azisamalira ndi kumanga misasa mozungulira tentiyo.
50 Mas ponha os levitas para cuidarem da Tenda Sagrada e de todos os seus móveis e objetos. Eles carregarão a Tenda e todo o seu equipamento, farão ali o serviço religioso e acamparão ao redor dela.
51 Pamene akusamutsa tentiyo, Alevi ndiwo aziyitsitsa, akafuna kuyimanganso, Alevi ndiwo aziyimiritsa. Wina aliyense amene adzayandikire tentiyo adzaphedwa.
51 Quando a Tenda tiver de ser transportada, os levitas a desarmarão e, quando for preciso acampar de novo, eles a armarão outra vez. Quem não for levita e chegar perto da Tenda deverá ser morto.
52 Aisraeli azimanga matenti awo mʼmagulumagulu, munthu aliyense ku gulu lake pansi pa mbendera yake.
52 Os outros israelitas ficarão cada um no seu próprio acampamento, perto da sua própria bandeira, de acordo com o seu grupo.
53 Alevi nawonso, azimanga matenti awo mozungulira tenti yopatulika kuti chilango chisagwere Aisraeli onse. Ndipo Alevi aziyangʼanira ndi kusamalira tenti yopatulikayo.”
53 Mas os levitas acamparão ao redor da Tenda para guardá-la a fim de que ninguém chegue perto, e assim eu não fique irado com o povo de Israel.
54 Choncho Aisraeli anachita monga Yehova analamulira Mose.
54 E o povo fez tudo como o Senhor havia ordenado a Moisés.

Ler em outra tradução

Comparar com outra