Salmos 94

NYA

1 Inu Yehova, ndinu Mulungu wobwezera chilango,

2 Nyamukani, Inu woweruza wa dziko lapansi;

3 Kodi mpaka liti anthu oyipa Inu Yehova,

4 Amakhuthula mawu onyada;

5 Amaphwanya anthu anu, Inu Yehova;

6 Amaphanso amayi a masiye ndi alendo okhala nawo mʼdziko;

7 Iwo amati, “Yehova sakuona;

8 Samalani, inu anthu opanda nzeru pakati pa anthu;

9 Kodi Iye amene anapanga khutu sangathe kumva?

10 Kodi Iye amene amalangiza mitundu ya anthu sangathenso kulanga?

11 Yehova amadziwa maganizo a munthu;

12 Wodala munthu amene Inu Yehova mumamulangiza,

13 mumamupumitsa pa nthawi ya mavuto,

14 Pakuti Yehova sadzawakana anthu ake;

15 Chiweruzo chidzakhazikikanso pa chilungamo,

16 Ndani adzadzuka chifukwa cha ine kulimbana ndi anthu oyipa?

17 Yehova akanapanda kundithandiza,

18 Ndikanena kuti, “Phazi langa likuterereka,”

19 Pamene nkhawa inakula mʼkati mwanga,

20 Kodi mpando waufumu woyipa ungathe kugwirizana nanu

21 Iwo amasonkhana pamodzi kulimbana ndi wolungama

22 Koma Yehova wakhala linga langa,

23 Iye adzawabwezera chifukwa cha machimo awo

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado