1 Yehova akulamulira, wavala ulemerero;
2 Mpando wanu waufumu unakhazikika kalekale;
3 Nyanja zakweza Inu Yehova,
4 Yehova ndi wamphamvu kupambana mkokomo wa madzi ambiri,
5 Malamulo anu Yehova ndi osasinthika;
NYA
1 Yehova akulamulira, wavala ulemerero;
2 Mpando wanu waufumu unakhazikika kalekale;
3 Nyanja zakweza Inu Yehova,
4 Yehova ndi wamphamvu kupambana mkokomo wa madzi ambiri,
5 Malamulo anu Yehova ndi osasinthika;