1 Nʼkwabwino kutamanda Yehova
2 Kulengeza chikondi chanu mmawa,
3 kuyimbira nyimbo choyimbira cha zingwe khumi
4 Pakuti Inu mumandisangalatsa ndi ntchito zanu, Inu Yehova;
5 Ndi yayikuludi ntchito yanu Yehova,
6 Munthu wopanda nzeru sadziwa,
7 kuti ngakhale anthu oyipa aphuka ngati udzu
8 Koma Inu Yehova, ndinu wokwezedwa kwamuyaya.
9 Zoonadi adani anu Yehova,
10 Inu mwakweza nyanga yanga ngati nyanga ya njati;
11 Maso anga aona kugonjetsedwa kwa olimbana nane,
12 Anthu olungama adzaphuka ngati mtengo wa mgwalangwa,
13 odzalidwa mʼnyumba ya Yehova,
14 Iwo adzaberekabe zipatso mu ukalamba wawo,
15 kulengeza kuti, “Yehova ndi wolungama;