Salmos 91

NYA

1 Iye amene amakhala mu mthunzi wa Wammwambamwamba

2 Ndidzanena za Yehova, “Iye ndiye pothawira panga ndi linga langa,

3 Ndithu, Iye adzakupulumutsa ku msampha wa mlenje

4 Adzakuphimba ndi nthenga zake,

5 Sudzachita mantha ndi zoopsa za usiku,

6 kapena mliri umene umayenda mu mdima,

7 Anthu 1,000 atha kufa pambali pako,

8 Udzapenya ndi maso ako

9 Pakuti wasankha Wammwambamwamba kukhala malo ako okhalamo;

10 Choncho palibe choyipa chimene chidzakugwera,

11 Pakuti adzalamulira angelo ake za iwe,

12 ndipo adzakunyamula ndi manja awo,

13 Udzapondaponda mkango ndi njoka,

14 “Chifukwa iye amandikonda,” akutero Yehova, “Ndidzamulanditsa;

15 Adzandiyitana, ndipo ndidzamuyankha;

16 Ndidzamupatsa moyo wautali

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado