1 Iye amene amakhala mu mthunzi wa Wammwambamwamba
2 Ndidzanena za Yehova, “Iye ndiye pothawira panga ndi linga langa,
3 Ndithu, Iye adzakupulumutsa ku msampha wa mlenje
4 Adzakuphimba ndi nthenga zake,
5 Sudzachita mantha ndi zoopsa za usiku,
6 kapena mliri umene umayenda mu mdima,
7 Anthu 1,000 atha kufa pambali pako,
8 Udzapenya ndi maso ako
9 Pakuti wasankha Wammwambamwamba kukhala malo ako okhalamo;
10 Choncho palibe choyipa chimene chidzakugwera,
11 Pakuti adzalamulira angelo ake za iwe,
12 ndipo adzakunyamula ndi manja awo,
13 Udzapondaponda mkango ndi njoka,
14 “Chifukwa iye amandikonda,” akutero Yehova, “Ndidzamulanditsa;
15 Adzandiyitana, ndipo ndidzamuyankha;
16 Ndidzamupatsa moyo wautali