Salmos 95

NYA

1 Bwerani, tiyeni timuyimbire Yehova mwachimwemwe,

2 Tiyeni tibwere pamaso pake ndi chiyamiko

3 Pakuti Yehova ndi Mulungu wamkulu,

4 Mʼmanja mwake muli maziko ozama a dziko lapansi,

5 Nyanja ndi yake, pakuti anayilenga ndi Iye,

6 Bwerani, tiyeni tiwerame pomulambira,

7 pakuti Iye ndiye Mulungu wathu

8 musawumitse mitima yanu monga momwe munachitira pa Meriba,

9 Kumene makolo anu anandiyesa ndi kundiputa,

10 Kwa zaka makumi anayi ndinali wokwiya ndi mʼbado umenewo;

11 Choncho ndili chikwiyire, ndinalumbira kuti,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado