1 Bwerani, tiyeni timuyimbire Yehova mwachimwemwe,
2 Tiyeni tibwere pamaso pake ndi chiyamiko
3 Pakuti Yehova ndi Mulungu wamkulu,
4 Mʼmanja mwake muli maziko ozama a dziko lapansi,
5 Nyanja ndi yake, pakuti anayilenga ndi Iye,
6 Bwerani, tiyeni tiwerame pomulambira,
7 pakuti Iye ndiye Mulungu wathu
8 musawumitse mitima yanu monga momwe munachitira pa Meriba,
9 Kumene makolo anu anandiyesa ndi kundiputa,
10 Kwa zaka makumi anayi ndinali wokwiya ndi mʼbado umenewo;
11 Choncho ndili chikwiyire, ndinalumbira kuti,