1 Imbirani Yehova nyimbo yatsopano;
2 Imbirani Yehova, tamandani dzina lake;
3 Lengezani ulemerero wake pakati pa mayiko,
4 Pakuti wamkulu ndi Yehova ndipo ndi woyenera kwambiri kumutamanda;
5 Pakuti milungu yonse ya anthu a mitundu ina ndi mafano,
6 Ulemu ndi ufumu zili pamaso pake,
7 Perekani kwa Yehova, inu mabanja a anthu a mitundu ina,
8 Perekani kwa Yehova ulemerero woyenera dzina lake;
9 Lambirani Yehova mu ulemerero wa chiyero chake;
10 Nenani pakati pa mitundu ya anthu, “Yehova akulamulira.”
11 Mayiko akumwamba asangalale, dziko lapansi likondwere;
12 minda ikondwere pamodzi ndi chilichonse chili mʼmenemo.
13 idzayimba pamaso pa Yehova,