Salmos 96

NYA

1 Imbirani Yehova nyimbo yatsopano;

2 Imbirani Yehova, tamandani dzina lake;

3 Lengezani ulemerero wake pakati pa mayiko,

4 Pakuti wamkulu ndi Yehova ndipo ndi woyenera kwambiri kumutamanda;

5 Pakuti milungu yonse ya anthu a mitundu ina ndi mafano,

6 Ulemu ndi ufumu zili pamaso pake,

7 Perekani kwa Yehova, inu mabanja a anthu a mitundu ina,

8 Perekani kwa Yehova ulemerero woyenera dzina lake;

9 Lambirani Yehova mu ulemerero wa chiyero chake;

10 Nenani pakati pa mitundu ya anthu, “Yehova akulamulira.”

11 Mayiko akumwamba asangalale, dziko lapansi likondwere;

12 minda ikondwere pamodzi ndi chilichonse chili mʼmenemo.

13 idzayimba pamaso pa Yehova,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado