1 Yehova akulamulira, dziko lapansi lisangalale;
2 Mitambo ndi mdima waukulu zamuzungulira;
3 Moto umapita patsogolo pake
4 Zingʼaningʼani zake zimawalitsa dziko lonse;
5 Mapiri amasungunuka ngati phula pamaso pa Yehova,
6 Mayiko akumwamba amalengeza za chilungamo chake,
7 Onse amene amalambira mafano osema amachititsidwa manyazi,
8 Ziyoni akumva ndipo akukondwera,
9 Pakuti Inu Yehova ndi Wammwambamwamba pa dziko lonse lapansi;
10 Iwo amene amakonda Yehova adane ndi zoyipa
11 Kuwala kumafika pa anthu olungama,
12 Kondwerani mwa Yehova Inu olungama