Salmos 98

NYA

1 Imbirani Yehova nyimbo yatsopano,

2 Yehova waonetsa chipulumutso chake

3 Iye wakumbukira chikondi chake

4 Fuwulani mwachimwemwe kwa Yehova, dziko lonse lapansi,

5 Imbirani Yehova nyimbo ndi zeze,

6 ndi malipenga ndi kuliza kwa nyanga ya nkhosa yayimuna

7 Nyanja ikokome pamodzi ndi zonse zili mʼmenemo,

8 Mitsinje iwombe mʼmanja mwawo,

9 izo ziyimbe pamaso pa Yehova,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado