1 Imbirani Yehova nyimbo yatsopano,
2 Yehova waonetsa chipulumutso chake
3 Iye wakumbukira chikondi chake
4 Fuwulani mwachimwemwe kwa Yehova, dziko lonse lapansi,
5 Imbirani Yehova nyimbo ndi zeze,
6 ndi malipenga ndi kuliza kwa nyanga ya nkhosa yayimuna
7 Nyanja ikokome pamodzi ndi zonse zili mʼmenemo,
8 Mitsinje iwombe mʼmanja mwawo,
9 izo ziyimbe pamaso pa Yehova,