1 Yehova akulamulira,
2 Mʼziyoni wamkulu ndi Yehova;
3 Anthu atamande dzina lanu lalikulu ndi loopsa kwambiri,
4 Mfumu yamphamvu, iyo imakonda chilungamo
5 Kwezani Yehova Mulungu wathu
6 Mose ndi Aaroni anali ena mwa ansembe ake,
7 Iye anayankhula nawo kuchokera mʼchipilala cha mtambo;
8 Inu Yehova Mulungu wathu,
9 Kwezani Yehova Mulungu wathu