Salmos 99

NYA

1 Yehova akulamulira,

2 Mʼziyoni wamkulu ndi Yehova;

3 Anthu atamande dzina lanu lalikulu ndi loopsa kwambiri,

4 Mfumu yamphamvu, iyo imakonda chilungamo

5 Kwezani Yehova Mulungu wathu

6 Mose ndi Aaroni anali ena mwa ansembe ake,

7 Iye anayankhula nawo kuchokera mʼchipilala cha mtambo;

8 Inu Yehova Mulungu wathu,

9 Kwezani Yehova Mulungu wathu

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado