1 Fuwulani kwa Yehova mwachimwemwe, inu dziko lonse lapansi.
2 Mulambireni Yehova mosangalala;
3 Dziwani kuti Yehova ndi Mulungu.
4 Lowani ku zipata zake ndi chiyamiko
5 Pakuti Yehova ndi wabwino ndipo chikondi chake ndi chamuyaya;
NYA
1 Fuwulani kwa Yehova mwachimwemwe, inu dziko lonse lapansi.
2 Mulambireni Yehova mosangalala;
3 Dziwani kuti Yehova ndi Mulungu.
4 Lowani ku zipata zake ndi chiyamiko
5 Pakuti Yehova ndi wabwino ndipo chikondi chake ndi chamuyaya;