Salmos 100

NYA

1 Fuwulani kwa Yehova mwachimwemwe, inu dziko lonse lapansi.

2 Mulambireni Yehova mosangalala;

3 Dziwani kuti Yehova ndi Mulungu.

4 Lowani ku zipata zake ndi chiyamiko

5 Pakuti Yehova ndi wabwino ndipo chikondi chake ndi chamuyaya;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado