1 Ndidzayimba za chikondi ndi chiweruzo chanu cholungama;
2 Ndidzatsata njira yolungama;
3 Sindidzayika chinthu chilichonse choyipa
4 Anthu a mtima wokhota adzakhala kutali ndi ine;
5 Aliyense wosinjirira mnansi wake mseri
6 Maso anga adzakhala pa okhulupirika mʼdziko,
7 Aliyense wochita chinyengo
8 Mmawa uliwonse ndidzatontholetsa anthu