1 Yehova imvani pemphero langa;
2 Musandibisire nkhope yanu
3 Pakuti masiku anga akupita ngati utsi;
4 Mtima wanga wakanthidwa ndipo ukufota ngati udzu;
5 Chifukwa cha kubuwula kwanga kofuwula
6 Ndili ngati kadzidzi wa ku chipululu,
7 Ndimagona osapeza tulo; ndakhala
8 Tsiku lonse adani anga amandichita chipongwe;
9 Pakuti ndimadya phulusa ngati chakudya changa
10 chifukwa cha ukali wanu waukulu,
11 Masiku anga ali ngati mthunzi wa kumadzulo;
12 Koma Inu Yehova, muli pa mpando wanu waufumu kwamuyaya;
13 Inu mudzadzuka ndi kuchitira chifundo Ziyoni
14 Pakuti miyala yake ndi yokondedwa kwa atumiki anu;
15 Mitundu ya anthu idzaopa dzina la Yehova,
16 Pakuti Yehova adzamanganso Ziyoni
17 Iye adzayankha pemphero la anthu otayika;
18 Zimenezi zilembedwe chifukwa cha mibado ya mʼtsogolo,
19 “Yehova anayangʼana pansi kuchokera ku malo ake opatulika mmwamba,
20 kuti amve kubuwula kwa anthu a mʼndende,
21 Kotero dzina la Yehova lidzalengezedwa mu Ziyoni
22 pamene mitundu ya anthu ndi maufumu
23 Iye anathyola mphamvu zanga pa nthawi ya moyo wanga;
24 Choncho Ine ndinati:
25 Pachiyambi Inu munakhazikitsa maziko a dziko lapansi
26 Izi zidzatha, koma Inu mudzakhalapo;
27 Koma Inu simusintha,
28 Ana a atumiki anu adzakhala pamaso panu;