Salmos 102

NYA

1 Yehova imvani pemphero langa;

2 Musandibisire nkhope yanu

3 Pakuti masiku anga akupita ngati utsi;

4 Mtima wanga wakanthidwa ndipo ukufota ngati udzu;

5 Chifukwa cha kubuwula kwanga kofuwula

6 Ndili ngati kadzidzi wa ku chipululu,

7 Ndimagona osapeza tulo; ndakhala

8 Tsiku lonse adani anga amandichita chipongwe;

9 Pakuti ndimadya phulusa ngati chakudya changa

10 chifukwa cha ukali wanu waukulu,

11 Masiku anga ali ngati mthunzi wa kumadzulo;

12 Koma Inu Yehova, muli pa mpando wanu waufumu kwamuyaya;

13 Inu mudzadzuka ndi kuchitira chifundo Ziyoni

14 Pakuti miyala yake ndi yokondedwa kwa atumiki anu;

15 Mitundu ya anthu idzaopa dzina la Yehova,

16 Pakuti Yehova adzamanganso Ziyoni

17 Iye adzayankha pemphero la anthu otayika;

18 Zimenezi zilembedwe chifukwa cha mibado ya mʼtsogolo,

19 “Yehova anayangʼana pansi kuchokera ku malo ake opatulika mmwamba,

20 kuti amve kubuwula kwa anthu a mʼndende,

21 Kotero dzina la Yehova lidzalengezedwa mu Ziyoni

22 pamene mitundu ya anthu ndi maufumu

23 Iye anathyola mphamvu zanga pa nthawi ya moyo wanga;

24 Choncho Ine ndinati:

25 Pachiyambi Inu munakhazikitsa maziko a dziko lapansi

26 Izi zidzatha, koma Inu mudzakhalapo;

27 Koma Inu simusintha,

28 Ana a atumiki anu adzakhala pamaso panu;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado