Salmos 103

NYA

1 Tamanda Yehova, iwe moyo wanga;

2 Tamanda Yehova, iwe moyo wanga,

3 Amene amakhululuka machimo ako onse

4 amene awombola moyo wako ku dzenje

5 amene akwaniritsa zokhumba zako ndi zinthu zabwino,

6 Yehova amachita chilungamo

7 Iye anadziwitsa Mose njira zake,

8 Yehova ndi wachifundo ndi wokoma mtima,

9 Iye sadzatsutsa nthawi zonse,

10 satichitira molingana ndi machimo athu,

11 Pakuti monga kumwamba kuli kutali ndi dziko lapansi,

12 monga kummawa kutalikirana ndi kumadzulo,

13 Monga bambo amachitira chifundo ana ake,

14 pakuti Iye amadziwa momwe tinawumbidwira,

15 Kunena za munthu, masiku ake ali ngati udzu,

16 koma mphepo imawombapo ndipo silionekanso

17 Koma kuchokera muyaya mpaka muyaya

18 iwo amene amasunga pangano lake

19 Yehova wakhazikitsa mpando wake waufumu mmwamba

20 Tamandani Yehova, inu angelo ake,

21 Tamandani Yehova, zolengedwa zonse zakumwamba,

22 Tamandani Yehova, ntchito yake yonse

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado