1 Tamanda Yehova, iwe moyo wanga;
2 Tamanda Yehova, iwe moyo wanga,
3 Amene amakhululuka machimo ako onse
4 amene awombola moyo wako ku dzenje
5 amene akwaniritsa zokhumba zako ndi zinthu zabwino,
6 Yehova amachita chilungamo
7 Iye anadziwitsa Mose njira zake,
8 Yehova ndi wachifundo ndi wokoma mtima,
9 Iye sadzatsutsa nthawi zonse,
10 satichitira molingana ndi machimo athu,
11 Pakuti monga kumwamba kuli kutali ndi dziko lapansi,
12 monga kummawa kutalikirana ndi kumadzulo,
13 Monga bambo amachitira chifundo ana ake,
14 pakuti Iye amadziwa momwe tinawumbidwira,
15 Kunena za munthu, masiku ake ali ngati udzu,
16 koma mphepo imawombapo ndipo silionekanso
17 Koma kuchokera muyaya mpaka muyaya
18 iwo amene amasunga pangano lake
19 Yehova wakhazikitsa mpando wake waufumu mmwamba
20 Tamandani Yehova, inu angelo ake,
21 Tamandani Yehova, zolengedwa zonse zakumwamba,
22 Tamandani Yehova, ntchito yake yonse