1 Tamandani Yehova.
2 Mutamandeni, inu angelo ake onse,
3 Mutamandeni, inu dzuwa ndi mwezi,
4 Mutamandeni, inu thambo la kumwambamwamba
5 Zonse zitamande dzina la Yehova
6 Iye anaziyika pa malo ake ku nthawi za nthawi;
7 Tamandani Yehova pa dziko lapansi,
8 inu zingʼaningʼani ndi matalala, chipale ndi mitambo,
9 inu mapiri ndi zitunda zonse,
10 inu nyama zakuthengo ndi ngʼombe zonse,
11 Inu mafumu a dziko lapansi ndi anthu a mitundu yonse,
12 Inu anyamata ndi anamwali,
13 Onsewo atamande dzina la Yehova
14 Iye wakwezera nyanga anthu ake,