Salmos 148

NYA

1 Tamandani Yehova.

2 Mutamandeni, inu angelo ake onse,

3 Mutamandeni, inu dzuwa ndi mwezi,

4 Mutamandeni, inu thambo la kumwambamwamba

5 Zonse zitamande dzina la Yehova

6 Iye anaziyika pa malo ake ku nthawi za nthawi;

7 Tamandani Yehova pa dziko lapansi,

8 inu zingʼaningʼani ndi matalala, chipale ndi mitambo,

9 inu mapiri ndi zitunda zonse,

10 inu nyama zakuthengo ndi ngʼombe zonse,

11 Inu mafumu a dziko lapansi ndi anthu a mitundu yonse,

12 Inu anyamata ndi anamwali,

13 Onsewo atamande dzina la Yehova

14 Iye wakwezera nyanga anthu ake,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado