1 Tamandani Yehova.
2 Israeli asangalale mwa mlengi wake;
3 Atamande dzina lake povina
4 Pakuti Yehova amakondwera ndi anthu ake;
5 Oyera mtima asangalale mu ulemu wake
6 Matamando a Mulungu akhale pakamwa pawo,
7 kubwezera chilango anthu a mitundu ina,
8 kumanga mafumu awo ndi zingwe,
9 kuchita zimene zinalembedwa zotsutsana nawo