1 Tamandani Yehova.
2 Yehova akumanga Yerusalemu;
3 Akutsogolera anthu osweka mtima
4 Amadziwa chiwerengero cha nyenyezi,
5 Yehova ndi wamkulu ndi wamphamvu kwambiri;
6 Yehova amagwiriziza anthu odzichepetsa,
7 Imbirani Yehova ndi mayamiko;
8 Iye amaphimba mlengalenga ndi mitambo;
9 Iye amapereka chakudya kwa ngʼombe
10 Chikondwerero chake sichili mʼmphamvu za kavalo,
11 Yehova amakondwera ndi amene amamuopa,
12 Lemekeza Yehova, iwe Yerusalemu;
13 pakuti Iye amalimbitsa mipiringidzo ya zipata zako
14 Iye amabweretsa mtendere mʼmalire mwako
15 Iyeyo amapereka lamulo pa dziko lapansi;
16 Amagwetsa chisanu ngati ubweya
17 Amagwetsa matalala ngati miyala.
18 Amatumiza mawu ake ndipo chisanucho chimasungunuka;
19 Iye anawulula mawu ake kwa Yakobo,
20 Sanachitepo zimenezi kwa mtundu wina uliwonse wa anthu;