Salmos 147

NYA

1 Tamandani Yehova.

2 Yehova akumanga Yerusalemu;

3 Akutsogolera anthu osweka mtima

4 Amadziwa chiwerengero cha nyenyezi,

5 Yehova ndi wamkulu ndi wamphamvu kwambiri;

6 Yehova amagwiriziza anthu odzichepetsa,

7 Imbirani Yehova ndi mayamiko;

8 Iye amaphimba mlengalenga ndi mitambo;

9 Iye amapereka chakudya kwa ngʼombe

10 Chikondwerero chake sichili mʼmphamvu za kavalo,

11 Yehova amakondwera ndi amene amamuopa,

12 Lemekeza Yehova, iwe Yerusalemu;

13 pakuti Iye amalimbitsa mipiringidzo ya zipata zako

14 Iye amabweretsa mtendere mʼmalire mwako

15 Iyeyo amapereka lamulo pa dziko lapansi;

16 Amagwetsa chisanu ngati ubweya

17 Amagwetsa matalala ngati miyala.

18 Amatumiza mawu ake ndipo chisanucho chimasungunuka;

19 Iye anawulula mawu ake kwa Yakobo,

20 Sanachitepo zimenezi kwa mtundu wina uliwonse wa anthu;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado