1 Tamandani Yehova.
2 Ndidzatamanda Yehova ndi moyo wanga wonse;
3 Musamadalire mafumu,
4 Pamene mizimu yawo yachoka, iwo amabwerera ku dothi;
5 Wodala ndi amene thandizo lake ndi
6 Wolenga kumwamba ndi dziko lapansi,
7 Iye amachitira chilungamo anthu oponderezedwa
8 Yehova amatsekula maso anthu osaona,
9 Yehova amasamalira alendo
10 Yehova ndiye Mfumu mpaka muyaya,