1 Ine ndidzakutamandani, Inu Yehova, ndi mtima wanga wonse;
2 Ndidzakondwa ndi kusangalala mwa inu;
3 Adani anga amathawa,
4 Pakuti Inu mwatsimikiza za kulungama kwanga ndi mlandu wanga;
5 Mwadzudzula mitundu ya anthu ndipo mwawononga anthu oyipa;
6 Chiwonongeko chosatha chagwera adani,
7 Yehova akulamulira kwamuyaya;
8 Iye adzaweruza dziko mwachilungamo;
9 Yehova ndiye kothawirako kwa opsinjika mtima,
10 Iwo amene amadziwa dzina lanu adzadalira Inu,
11 Imbani nyimbo zamatamando kwa Yehova, ali pa mpando waufumu mu Ziyoni;
12 Pakuti Iye amene amabwezera chilango akupha anzawo wakumbukira;
13 Inu Yehova, onani momwe adani anga akundizunzira!
14 kuti ndilengeze za matamando anu
15 Mitundu ya anthu yagwa mʼdzenje limene yakumba;
16 Yehova amadziwika ndi chilungamo chake;
17 Oyipa amabwerera ku manda,
18 Koma osowa sadzayiwalika nthawi zonse,
19 Dzukani Inu Yehova, musalole munthu kuti apambane;
20 Akantheni ndi mantha aakulu, Inu Yehova;