Salmos 9

NYA

1 Ine ndidzakutamandani, Inu Yehova, ndi mtima wanga wonse;

2 Ndidzakondwa ndi kusangalala mwa inu;

3 Adani anga amathawa,

4 Pakuti Inu mwatsimikiza za kulungama kwanga ndi mlandu wanga;

5 Mwadzudzula mitundu ya anthu ndipo mwawononga anthu oyipa;

6 Chiwonongeko chosatha chagwera adani,

7 Yehova akulamulira kwamuyaya;

8 Iye adzaweruza dziko mwachilungamo;

9 Yehova ndiye kothawirako kwa opsinjika mtima,

10 Iwo amene amadziwa dzina lanu adzadalira Inu,

11 Imbani nyimbo zamatamando kwa Yehova, ali pa mpando waufumu mu Ziyoni;

12 Pakuti Iye amene amabwezera chilango akupha anzawo wakumbukira;

13 Inu Yehova, onani momwe adani anga akundizunzira!

14 kuti ndilengeze za matamando anu

15 Mitundu ya anthu yagwa mʼdzenje limene yakumba;

16 Yehova amadziwika ndi chilungamo chake;

17 Oyipa amabwerera ku manda,

18 Koma osowa sadzayiwalika nthawi zonse,

19 Dzukani Inu Yehova, musalole munthu kuti apambane;

20 Akantheni ndi mantha aakulu, Inu Yehova;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado