Salmos 8

NYA

1 Inu Yehova Ambuye athu,

2 Kuchokera mʼkamwa mwa ana ndi makanda,

3 Pamene ndilingalira za mayiko anu akumwamba,

4 munthu ndani kuti Inu mumamukumbukira,

5 Inu munamupanga kukhala wocheperapo kusiyana ndi zolengedwa zakumwamba

6 Inu munamuyika wolamulira ntchito ya manja anu;

7 nkhosa, mbuzi ndi ngʼombe pamodzi

8 mbalame zamlengalenga

9 Inu Yehova, Ambuye athu,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado