1 Inu Yehova Ambuye athu,
2 Kuchokera mʼkamwa mwa ana ndi makanda,
3 Pamene ndilingalira za mayiko anu akumwamba,
4 munthu ndani kuti Inu mumamukumbukira,
5 Inu munamupanga kukhala wocheperapo kusiyana ndi zolengedwa zakumwamba
6 Inu munamuyika wolamulira ntchito ya manja anu;
7 nkhosa, mbuzi ndi ngʼombe pamodzi
8 mbalame zamlengalenga
9 Inu Yehova, Ambuye athu,