Salmos 7

NYA

1 Inu Yehova Mulungu wanga, Ine ndikuthawira kwa Inu;

2 mwina angandikadzule ngati mkango,

3 Inu Yehova Mulungu wanga,

4 ngati ndachita zoyipa kwa iye amene ndili naye pa mtendere,

5 pamenepo lolani adani anga andithamangitse ndi kundipitirira,

6 Nyamukani Yehova, mu mkwiyo wanu;

7 Lolani gulu la anthu a mitundu ina lisonkhane mokuzungulirani.

8 Yehova aweruzeni anthu a mitundu inayo.

9 Inu Mulungu wolungama,

10 Chishango changa ndi Mulungu Wammwambamwamba,

11 Mulungu amaweruza molungama,

12 Ngati munthu satembenuka,

13 Mulungu wakonza zida zake zoopsa;

14 Taonani, munthu woyipa amalingalira zoyipa zokhazokha nthawi zonse.

15 Iye amene akumba dzenje ndi kulizamitsa

16 Mavuto amene amayambitsa amamubwerera mwini;

17 Ine ndidzayamika Yehova chifukwa cha chilungamo chake;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado