1 Inu Yehova Mulungu wanga, Ine ndikuthawira kwa Inu;
2 mwina angandikadzule ngati mkango,
3 Inu Yehova Mulungu wanga,
4 ngati ndachita zoyipa kwa iye amene ndili naye pa mtendere,
5 pamenepo lolani adani anga andithamangitse ndi kundipitirira,
6 Nyamukani Yehova, mu mkwiyo wanu;
7 Lolani gulu la anthu a mitundu ina lisonkhane mokuzungulirani.
8 Yehova aweruzeni anthu a mitundu inayo.
9 Inu Mulungu wolungama,
10 Chishango changa ndi Mulungu Wammwambamwamba,
11 Mulungu amaweruza molungama,
12 Ngati munthu satembenuka,
13 Mulungu wakonza zida zake zoopsa;
14 Taonani, munthu woyipa amalingalira zoyipa zokhazokha nthawi zonse.
15 Iye amene akumba dzenje ndi kulizamitsa
16 Mavuto amene amayambitsa amamubwerera mwini;
17 Ine ndidzayamika Yehova chifukwa cha chilungamo chake;