Salmos 6

NYA

1 Inu Yehova, musandidzudzule mu mkwiyo wanu,

2 Ndichitireni chifundo Inu Yehova, pakuti ndalefuka;

3 Moyo wanga uli pa mazunzo aakulu.

4 Tembenukani Inu Yehova, ndipo mundilanditse;

5 Palibe amene amakukumbukirani pamene wamwalira;

6 Ine ndatopa ndi kubuwula;

7 Maso anga atupa chifukwa cha chisoni;

8 Chokani kwa ine inu nonse amene mumachita zoyipa,

9 Yehova wamva kupempha kwanga kofuna chifundo;

10 Adani anga onse adzachita manyazi ndipo adzakhala ndi mantha;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado