1 Inu Yehova, musandidzudzule mu mkwiyo wanu,
2 Ndichitireni chifundo Inu Yehova, pakuti ndalefuka;
3 Moyo wanga uli pa mazunzo aakulu.
4 Tembenukani Inu Yehova, ndipo mundilanditse;
5 Palibe amene amakukumbukirani pamene wamwalira;
6 Ine ndatopa ndi kubuwula;
7 Maso anga atupa chifukwa cha chisoni;
8 Chokani kwa ine inu nonse amene mumachita zoyipa,
9 Yehova wamva kupempha kwanga kofuna chifundo;
10 Adani anga onse adzachita manyazi ndipo adzakhala ndi mantha;