1 Tcherani khutu ku mawu anga, Inu Yehova,
2 Mverani kulira kwanga kofuna thandizo,
3 Mmawa, Yehova mumamva mawu anga;
4 Inu si Mulungu amene mumasangalala ndi zoyipa;
5 Onyada sangathe kuyima pamaso panu;
6 Mumawononga iwo amene amanena mabodza;
7 Koma Ine, mwa chifundo chanu chachikulu,
8 Tsogolereni Inu Yehova, mwa chilungamo chanu
9 Palibe mawu ochokera mʼkamwa mwawo amene angadalirike;
10 Lengezani kuti ndi olakwa, Inu Mulungu!
11 Koma lolani kuti onse amene apeza chitetezo mwa Inu akondwere;
12 Ndithu, Inu Yehova, mumadalitsa olungama;