Salmos 5

NYA

1 Tcherani khutu ku mawu anga, Inu Yehova,

2 Mverani kulira kwanga kofuna thandizo,

3 Mmawa, Yehova mumamva mawu anga;

4 Inu si Mulungu amene mumasangalala ndi zoyipa;

5 Onyada sangathe kuyima pamaso panu;

6 Mumawononga iwo amene amanena mabodza;

7 Koma Ine, mwa chifundo chanu chachikulu,

8 Tsogolereni Inu Yehova, mwa chilungamo chanu

9 Palibe mawu ochokera mʼkamwa mwawo amene angadalirike;

10 Lengezani kuti ndi olakwa, Inu Mulungu!

11 Koma lolani kuti onse amene apeza chitetezo mwa Inu akondwere;

12 Ndithu, Inu Yehova, mumadalitsa olungama;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado