1 Ndiyankheni pamene ndiyitana Inu,
2 Anthu inu, mpaka liti mudzakhala mukusandutsa ulemerero wanga kukhala manyazi?
3 Dziwani kuti Yehova wadziyikira padera anthu okhulupirika;
4 Kwiyani koma musachimwe;
5 Perekani nsembe zolungama
6 Ambiri akufunsa kuti, “Ndani angationetse chabwino chilichonse?”
7 Inu mwadzaza mtima wanga ndi chimwemwe chachikulu
8 Ine ndidzagona ndi kupeza tulo mwamtendere,