Salmos 4

NYA

1 Ndiyankheni pamene ndiyitana Inu,

2 Anthu inu, mpaka liti mudzakhala mukusandutsa ulemerero wanga kukhala manyazi?

3 Dziwani kuti Yehova wadziyikira padera anthu okhulupirika;

4 Kwiyani koma musachimwe;

5 Perekani nsembe zolungama

6 Ambiri akufunsa kuti, “Ndani angationetse chabwino chilichonse?”

7 Inu mwadzaza mtima wanga ndi chimwemwe chachikulu

8 Ine ndidzagona ndi kupeza tulo mwamtendere,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado