Salmos 3

NYA

1 Inu Yehova, achulukadi adani anga!

2 Ambiri akunena za ine kuti,

3 Koma Inu Yehova, ndinu chishango chonditeteza,

4 Kwa Yehova, Ine ndilira mofuwula

5 Ine ndimagona ndi kupeza tulo;

6 Sindidzaopa adani anga osawerengeka amene

7 Dzukani, Inu Yehova!

8 Chipulumutso chimachokera kwa Yehova.

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado