1 Inu Yehova, achulukadi adani anga!
2 Ambiri akunena za ine kuti,
3 Koma Inu Yehova, ndinu chishango chonditeteza,
4 Kwa Yehova, Ine ndilira mofuwula
5 Ine ndimagona ndi kupeza tulo;
6 Sindidzaopa adani anga osawerengeka amene
7 Dzukani, Inu Yehova!
8 Chipulumutso chimachokera kwa Yehova.