1 Nʼchifukwa chiyani anthu a mitundu ina akufuna kuchita chiwembu?
2 Mafumu a dziko lapansi akugwirizana nazo;
3 Iwo akunena kuti, “Tiyeni timasule magoli awo
4 Wokhala mmwamba akuseka;
5 Ndipo iye awadzudzula mu mkwiyo wake
6 “Ine ndakhazikitsa mfumu yanga
7 Ine ndidzalengeza zimene Yehova walamula:
8 Tandipempha,
9 Iweyo udzawalamulira ndi ndodo yaufumu yachitsulo;
10 Kotero, inu mafumu, chenjerani;
11 Tumikirani Yehova mwa mantha
12 Mpsopsoneni mwanayo kuti angakwiye;