Salmos 2

NYA

1 Nʼchifukwa chiyani anthu a mitundu ina akufuna kuchita chiwembu?

2 Mafumu a dziko lapansi akugwirizana nazo;

3 Iwo akunena kuti, “Tiyeni timasule magoli awo

4 Wokhala mmwamba akuseka;

5 Ndipo iye awadzudzula mu mkwiyo wake

6 “Ine ndakhazikitsa mfumu yanga

7 Ine ndidzalengeza zimene Yehova walamula:

8 Tandipempha,

9 Iweyo udzawalamulira ndi ndodo yaufumu yachitsulo;

10 Kotero, inu mafumu, chenjerani;

11 Tumikirani Yehova mwa mantha

12 Mpsopsoneni mwanayo kuti angakwiye;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado