Salmos 10

NYA

1 Nʼchifukwa chiyani Yehova mwayima patali?

2 Mwa kunyada kwake munthu woyipa asaka wofowoka,

3 Iye amatamandira zokhumba za mu mtima wake;

4 Mwa kunyada kwake woyipa safunafuna Mulungu;

5 Zinthu zake zimamuyendera bwino;

6 Iye amadziyankhulira kuti, “Palibe chimene chidzandigwedeze.

7 Mʼkamwa mwake mwadzaza matemberero, mabodza ndi zoopseza;

8 Iye amabisalira anthu pafupi ndi midzi,

9 Amabisalira anthu ngati mkango pa zitsamba.

10 Anthuwo amawapondaponda ndipo amakomoka;

11 Iye amati mu mtima mwake, “Mulungu wayiwala,

12 Dzukani Yehova! Onetsani dzanja lanu Inu Mulungu.

13 Nʼchifukwa chiyani munthu woyipa amachitira chipongwe Mulungu?

14 Komatu Inu Mulungu, mumazindikira mavuto ndi zosautsa,

15 Thyolani dzanja la woyipitsitsa ndi la munthu woyipa;

16 Yehova ndi Mfumu kwamuyaya;

17 Mumamva Inu Yehova, zokhumba za osautsidwa;

18 Kuteteza ana amasiye ndi oponderezedwa,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado