Salmos 88

NYA

1 Inu Yehova, Mulungu amene mumandipulumutsa,

2 Pemphero langa lifike pamaso panu;

3 Pakuti ndili ndi mavuto ambiri

4 Ndikuwerengedwa pamodzi ndi iwo amene akutsikira ku dzenje;

5 Ndayikidwa pambali pamodzi ndi anthu akufa,

6 Mwandiyika pansi pa dzenje penipeni,

7 Ukali wanu ukundipsinja kwambiri,

8 Mwandichotsa pakati pa abwenzi anga enieni

9 maso anga ada ndi chisoni.

10 Kodi mumaonetsa zozizwitsa zanu kwa anthu akufa?

11 Kodi chikondi chanu chimalalikidwa mʼmanda,

12 Kodi zozizwitsa zanu zimadziwika ku malo a mdima,

13 Inu Yehova, Ine ndimalirira thandizo;

14 Inu Yehova nʼchifukwa chiyani mukundikana

15 Kuyambira ubwana wanga ndakhala ndikuzunzika pafupi kufa;

16 Ukali wanu wandimiza;

17 Tsiku lonse zimandizungulira ngati chigumula;

18 Inu mwatenga anzanga ndi okondedwa anga kuwachotsa pamaso panga;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado