1 Iye wakhazikitsa maziko ake pa phiri loyera;
2 Yehova amakonda zipata za Ziyoni
3 Za ulemerero wako zimakambidwa,
4 “Ndidzanena za Rahabe ndi Babuloni
5 Ndithudi, za Ziyoni adzanena kuti,
6 Yehova adzalemba mʼbuku la kawundula wa anthu a mitundu ina:
7 Oyimba ndi ovina omwe adzati,