Salmos 86

NYA

1 Ndimvereni Yehova ndipo mundiyankhe,

2 Yangʼanirani moyo wanga, pakuti ndine wodzipereka kwa Inu.

3 Mundichitire chifundo, Inu Ambuye,

4 Bweretsani chimwemwe kwa mtumiki wanu, Ambuye,

5 Inu Ambuye, ndinu wokhululuka ndi wabwino,

6 Yehova imvani pemphero langa;

7 Pa tsiku la mavuto anga ndidzayitana Inu,

8 Pakati pa milungu palibe wina wofanana nanu Ambuye;

9 Mitundu yonse ya anthu imene munayipanga

10 Pakuti ndinu wamkulu ndipo mumachita zodabwitsa;

11 Ndiphunzitseni njira yanu Yehova,

12 Ndidzakutamandani Ambuye Mulungu wanga, ndi mtima wanga wonse;

13 Pakuti chikondi chanu nʼchachikulu kwa ine;

14 Inu Mulungu wanga, anthu odzikuza akundithira nkhondo;

15 Koma Ambuye ndinu Mulungu wachifundo ndi wokoma mtima,

16 Tembenukirani kwa ine ndipo ndichitireni chifundo;

17 Mundionetse chizindikiro cha ubwino wanu

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado