Salmos 85

NYA

1 Yehova munakomera mtima dziko lanu;

2 Munakhululukira mphulupulu za anthu anu

3 Munayika pambali ukali wanu wonse

4 Tibwezeretseninso mwakale Inu Mulungu Mpulumutsi wathu,

5 Kodi mudzatikwiyira mpaka liti?

6 Kodi simudzatitsitsimutsanso,

7 Tionetseni chikondi chanu chosatha, Inu Yehova,

8 Ndidzamvetsera zimene Yehova Mulungu adzanena;

9 Ndithu chipulumutso chake chili pafupi ndi iwo amene amaopa Iye,

10 Chikondi ndi kukhulupirika zimakumana pamodzi;

11 Kukhulupirika kumatumphuka kuchokera ku dziko lapansi,

12 Ndithu Yehova adzapereka chimene chili chabwino,

13 Wolungama amapita patsogolo pake

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado