1 Yehova munakomera mtima dziko lanu;
2 Munakhululukira mphulupulu za anthu anu
3 Munayika pambali ukali wanu wonse
4 Tibwezeretseninso mwakale Inu Mulungu Mpulumutsi wathu,
5 Kodi mudzatikwiyira mpaka liti?
6 Kodi simudzatitsitsimutsanso,
7 Tionetseni chikondi chanu chosatha, Inu Yehova,
8 Ndidzamvetsera zimene Yehova Mulungu adzanena;
9 Ndithu chipulumutso chake chili pafupi ndi iwo amene amaopa Iye,
10 Chikondi ndi kukhulupirika zimakumana pamodzi;
11 Kukhulupirika kumatumphuka kuchokera ku dziko lapansi,
12 Ndithu Yehova adzapereka chimene chili chabwino,
13 Wolungama amapita patsogolo pake