1 Malo anu okhalamo ndi okomadi,
2 Moyo wanga ukulakalaka, mpaka kukomoka,
3 Ngakhale timba wapeza nyumba yokhalamo,
4 Odala amene amakhala mʼNyumba yanu;
5 Odala amene mphamvu yawo ili mwa Inu,
6 Pamene akudutsa chigwa cha Baka,
7 Iwo amanka nakulirakulira mphamvu
8 Imvani pemphero langa, Inu Yehova Mulungu Wamphamvuzonse;
9 Yangʼanani chishango chathu, Inu Mulungu;
10 Nʼkwabwino kukhala mʼmabwalo anu tsiku limodzi
11 Pakuti Yehova Mulungu ndi dzuwa ndi chishango;
12 Inu Yehova Wamphamvuzonse,