Salmos 84

NYA

1 Malo anu okhalamo ndi okomadi,

2 Moyo wanga ukulakalaka, mpaka kukomoka,

3 Ngakhale timba wapeza nyumba yokhalamo,

4 Odala amene amakhala mʼNyumba yanu;

5 Odala amene mphamvu yawo ili mwa Inu,

6 Pamene akudutsa chigwa cha Baka,

7 Iwo amanka nakulirakulira mphamvu

8 Imvani pemphero langa, Inu Yehova Mulungu Wamphamvuzonse;

9 Yangʼanani chishango chathu, Inu Mulungu;

10 Nʼkwabwino kukhala mʼmabwalo anu tsiku limodzi

11 Pakuti Yehova Mulungu ndi dzuwa ndi chishango;

12 Inu Yehova Wamphamvuzonse,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado