Salmos 83

NYA

1 Inu Mulungu musakhale chete;

2 Onani adani anu akuchita chiwawa,

3 Mochenjera iwo akukambirana za chiwembu kutsutsana ndi anthu anu;

4 Iwo akunena kuti, “Bwerani” akutero, “Tiyeni tiwononge mtundu wonsewu

5 Ndi mtima umodzi akukonzekera chiwembu;

6 Matenti a Edomu ndi Aismaeli,

7 Agebala, Aamoni ndi Aamaleki,

8 Ngakhalenso Aasiriya aphatikizana nawo

9 Muwachitire zomwe munachitira Amidiyani,

10 Amene anawonongedwa ku Endori

11 Anthu awo otchuka muwachite zomwe munachita Orebu ndi Zeebu

12 amene anati, “Tiyeni tilande dziko

13 Muwasandutse fumbi lowuluka, Inu Mulungu wanga,

14 Monga moto umatentha nkhalango,

15 kotero muwathamangitse ndi mphepo yamkuntho,

16 Muphimbe nkhope zawo ndi manyazi

17 Achite manyazi ndi mantha nthawi zonse;

18 Adziwe kuti Inu amene dzina lanu ndi Yehova,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado