1 Inu Mulungu musakhale chete;
2 Onani adani anu akuchita chiwawa,
3 Mochenjera iwo akukambirana za chiwembu kutsutsana ndi anthu anu;
4 Iwo akunena kuti, “Bwerani” akutero, “Tiyeni tiwononge mtundu wonsewu
5 Ndi mtima umodzi akukonzekera chiwembu;
6 Matenti a Edomu ndi Aismaeli,
7 Agebala, Aamoni ndi Aamaleki,
8 Ngakhalenso Aasiriya aphatikizana nawo
9 Muwachitire zomwe munachitira Amidiyani,
10 Amene anawonongedwa ku Endori
11 Anthu awo otchuka muwachite zomwe munachita Orebu ndi Zeebu
12 amene anati, “Tiyeni tilande dziko
13 Muwasandutse fumbi lowuluka, Inu Mulungu wanga,
14 Monga moto umatentha nkhalango,
15 kotero muwathamangitse ndi mphepo yamkuntho,
16 Muphimbe nkhope zawo ndi manyazi
17 Achite manyazi ndi mantha nthawi zonse;
18 Adziwe kuti Inu amene dzina lanu ndi Yehova,