1 Mulungu akutsogolera msonkhano waukulu;
2 “Mudzateteza osalungama mpaka liti,
3 Tetezani anthu ofowoka ndi amasiye;
4 Landitsani anthu ofowoka ndi osowa;
5 “Iwo sadziwa kanthu, sazindikira kalikonse.
6 “Ndinati, ‘Inu ndinu Mulungu,
7 Koma mudzafa ngati anthu wamba;
8 Dzukani Inu Mulungu, weruzani dziko lapansi,