Salmos 82

NYA

1 Mulungu akutsogolera msonkhano waukulu;

2 “Mudzateteza osalungama mpaka liti,

3 Tetezani anthu ofowoka ndi amasiye;

4 Landitsani anthu ofowoka ndi osowa;

5 “Iwo sadziwa kanthu, sazindikira kalikonse.

6 “Ndinati, ‘Inu ndinu Mulungu,

7 Koma mudzafa ngati anthu wamba;

8 Dzukani Inu Mulungu, weruzani dziko lapansi,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado