Salmos 80

NYA

1 Tcherani khutu Inu mʼbusa wa Israeli,

2 kwa Efereimu, Benjamini ndi Manase.

3 Tibwezereni mwakale Inu Mulungu;

4 Inu Mulungu Wamphamvuzonse,

5 Mwawadyetsa buledi wa misozi;

6 Mwachititsa kuti tikhale gwero la mikangano pakati pa anansi athu,

7 Tibwezereni mwakale Inu Mulungu Wamphamvuzonse,

8 Munatulutsa mpesa kuchoka ku Igupto;

9 Munawulimira munda wamphesawo,

10 Mapiri anaphimbidwa ndi mthunzi wake,

11 Unatambalitsa nthambi zake mpaka ku nyanja,

12 Chifukwa chiyani mwagwetsa makoma ake

13 Nguluwe zochokera mʼnkhalango zikuwononga

14 Bweraninso kwa ife Inu Mulungu Wamphamvuzonse!

15 muzu umene dzanja lanu lamanja ladzala,

16 Mpesa wanu wadulidwa ndi kutenthedwa ndi moto;

17 Dzanja lanu likhale pa munthu amene ali ku dzanja lanu lamanja,

18 Ndipo ife sitidzatembenukira kumbali kuchoka kwa Inu;

19 Tibwezereni mwakale Inu Yehova Mulungu Wamphamvuzonse

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado