Salmos 79

NYA

1 Inu Mulungu, anthu a mitundu ina alowerera mʼcholowa chanu;

2 Iwo anapereka mitembo ya atumiki anu

3 Akhetsa magazi monga madzi

4 Ife ndife chinthu chonyozeka kwa anansi athu,

5 Mpaka liti Inu Yehova? Kodi mudzakwiya mpaka muyaya?

6 Khuthulirani ukali wanu pa anthu a mitundu ina

7 pakuti iwo ameza Yakobo

8 Musatilange chifukwa cha machimo a makolo athu

9 Tithandizeni Inu Mulungu Mpulumutsi wathu,

10 Chifukwa chiyani anthu a mitundu ina akuti,

11 Kubuwula kwa anthu a mʼndende kufike pamaso panu;

12 Mubwezere kwa anansi athu kasanu nʼkawiri

13 Pamenepo ife anthu anu, nkhosa za pabusa panu,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado