1 Inu Mulungu, anthu a mitundu ina alowerera mʼcholowa chanu;
2 Iwo anapereka mitembo ya atumiki anu
3 Akhetsa magazi monga madzi
4 Ife ndife chinthu chonyozeka kwa anansi athu,
5 Mpaka liti Inu Yehova? Kodi mudzakwiya mpaka muyaya?
6 Khuthulirani ukali wanu pa anthu a mitundu ina
7 pakuti iwo ameza Yakobo
8 Musatilange chifukwa cha machimo a makolo athu
9 Tithandizeni Inu Mulungu Mpulumutsi wathu,
10 Chifukwa chiyani anthu a mitundu ina akuti,
11 Kubuwula kwa anthu a mʼndende kufike pamaso panu;
12 Mubwezere kwa anansi athu kasanu nʼkawiri
13 Pamenepo ife anthu anu, nkhosa za pabusa panu,