1 Ndinafuwulira Mulungu kupempha thandizo;
2 Pamene ndinali pa masautso ndinafunafuna Ambuye;
3 Ndinakumbukira Inu Mulungu, ndipo ndinabuwula;
4 Munagwira zikope zanga kuti ndisagone
5 Ndinaganizira za masiku akale,
6 Ndinakumbukira nyimbo zanga usiku.
7 “Kodi Ambuye adzatikana mpaka muyaya?
8 Kodi Chikondi chake chosatha chija chatheratu?
9 Kodi Mulungu wayiwala kukhala wokoma mtima?
10 Ndipo ndinaganiza, “Pa izi ine ndidzapemphanso:
11 Ine ndidzakumbukira ntchito za Yehova;
12 Ndidzakumbukira ntchito zanu
13 Njira zanu Mulungu ndi zoyera.
14 Inu ndinu Mulungu wochita zodabwitsa;
15 Ndi dzanja lanu lamphamvu munawombola anthu anu,
16 Madzi anakuonani Mulungu,
17 Mitambo inakhuthula madzi ake pansi,
18 Bingu lanu linamveka mʼmphepo ya kamvuluvulu,
19 Njira yanu inadutsa pa nyanja,
20 Inu munatsogolera anthu anu ngati gulu la nkhosa