1 Mulungu amadziwika mu Yuda;
2 Tenti yake ili mu Salemu,
3 Kumeneko Iye anathyola mivi yowuluka,
4 Wolemekezeka ndinu,
5 Anthu owuma mtima amagona atalandidwa chuma,
6 Pa kudzudzula kwanu, Inu Mulungu wa Yakobo,
7 Inu nokha ndiye muyenera kuopedwa.
8 Kuchokera kumwamba Inu munalengeza chiweruzo,
9 pamene Inu Mulungu munadzuka kuti muweruze,
10 Zoonadi, ukali wanu pa anthu umakubweretserani matamando
11 Chitani malumbiro kwa Yehova Mulungu wanu ndipo muwakwaniritse;
12 Iye amaswa mzimu wa olamulira;