Salmos 76

NYA

1 Mulungu amadziwika mu Yuda;

2 Tenti yake ili mu Salemu,

3 Kumeneko Iye anathyola mivi yowuluka,

4 Wolemekezeka ndinu,

5 Anthu owuma mtima amagona atalandidwa chuma,

6 Pa kudzudzula kwanu, Inu Mulungu wa Yakobo,

7 Inu nokha ndiye muyenera kuopedwa.

8 Kuchokera kumwamba Inu munalengeza chiweruzo,

9 pamene Inu Mulungu munadzuka kuti muweruze,

10 Zoonadi, ukali wanu pa anthu umakubweretserani matamando

11 Chitani malumbiro kwa Yehova Mulungu wanu ndipo muwakwaniritse;

12 Iye amaswa mzimu wa olamulira;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado