Salmos 75

NYA

1 Tikuthokoza Inu Mulungu,

2 Mumati, “Ine ndimayika nthawi yoyenera,

3 Pamene dziko lapansi ndi anthu ake onse anjenjemera,

4 Kwa odzitama ndikuti, ‘Musadzitamenso,’

5 Musatukule nyanga zanu motsutsana ndi kumwamba;

6 Kugamula milandu sikuchokera kummawa kapena kumadzulo

7 Koma ndi Mulungu amene amaweruza:

8 Mʼdzanja la Yehova muli chikho

9 Kunena za ine, ndidzalengeza izi kwamuyaya;

10 Ndidzadula nyanga za onse oyipa

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado