1 Tikuthokoza Inu Mulungu,
2 Mumati, “Ine ndimayika nthawi yoyenera,
3 Pamene dziko lapansi ndi anthu ake onse anjenjemera,
4 Kwa odzitama ndikuti, ‘Musadzitamenso,’
5 Musatukule nyanga zanu motsutsana ndi kumwamba;
6 Kugamula milandu sikuchokera kummawa kapena kumadzulo
7 Koma ndi Mulungu amene amaweruza:
8 Mʼdzanja la Yehova muli chikho
9 Kunena za ine, ndidzalengeza izi kwamuyaya;
10 Ndidzadula nyanga za onse oyipa