1 Nʼchifukwa chiyani mwatitaya ife kwamuyaya, Inu Mulungu?
2 Kumbukirani anthu amene munawagula kalekale,
3 Tembenuzani mapazi kuloza ku mabwinja awa amuyaya
4 Adani anu anabangula pa malo pamene Inu munkakumana nafe;
5 Iwo anachita ngati anthu oti anyamula mbendera zawo
6 Kenaka anaphwanya ndi nkhwangwa ndi akasemasema awo
7 Iwo anatentha malo anu opatulika mpaka kuwagwetsa pansi;
8 Ndipo anati mʼmitima yawo, “Tawatha kwathunthu.”
9 Ife sitinapatsidwe chizindikiro chodabwitsa;
10 Kodi mpaka liti, mdani adzanyoze Inu Mulungu?
11 Chifukwa chiyani mukubweza dzanja lanu lamanja?
12 Koma Inu Mulungu, ndinu Mfumu yanga kuyambira kalekale;
13 Ndinu amene munagawa nyanja ndi mphamvu yanu;
14 Ndinu amene munaphwanya mitu ya Leviyatani
15 Ndinu amene munatsekula akasupe ndi mitsinje,
16 Masana ndi anu ndipo usiku ndi wanunso;
17 Ndinu amene munakhazikitsa malire onse a dziko lapansi;
18 Kumbukirani momwe mdani wakunyozerani Inu Yehova,
19 Musapereke moyo wa nkhunda yanu ku zirombo zakuthengo;
20 Mukumbukire pangano lanu, pakuti malo obisika a mʼdziko
21 Musalole kuti osautsidwa abwerere mwamanyazi;
22 Dzukani Inu Mulungu ndipo dzitetezeni pa mlandu;
23 Musalekerere phokoso la otsutsana nanu,