Salmos 74

NYA

1 Nʼchifukwa chiyani mwatitaya ife kwamuyaya, Inu Mulungu?

2 Kumbukirani anthu amene munawagula kalekale,

3 Tembenuzani mapazi kuloza ku mabwinja awa amuyaya

4 Adani anu anabangula pa malo pamene Inu munkakumana nafe;

5 Iwo anachita ngati anthu oti anyamula mbendera zawo

6 Kenaka anaphwanya ndi nkhwangwa ndi akasemasema awo

7 Iwo anatentha malo anu opatulika mpaka kuwagwetsa pansi;

8 Ndipo anati mʼmitima yawo, “Tawatha kwathunthu.”

9 Ife sitinapatsidwe chizindikiro chodabwitsa;

10 Kodi mpaka liti, mdani adzanyoze Inu Mulungu?

11 Chifukwa chiyani mukubweza dzanja lanu lamanja?

12 Koma Inu Mulungu, ndinu Mfumu yanga kuyambira kalekale;

13 Ndinu amene munagawa nyanja ndi mphamvu yanu;

14 Ndinu amene munaphwanya mitu ya Leviyatani

15 Ndinu amene munatsekula akasupe ndi mitsinje,

16 Masana ndi anu ndipo usiku ndi wanunso;

17 Ndinu amene munakhazikitsa malire onse a dziko lapansi;

18 Kumbukirani momwe mdani wakunyozerani Inu Yehova,

19 Musapereke moyo wa nkhunda yanu ku zirombo zakuthengo;

20 Mukumbukire pangano lanu, pakuti malo obisika a mʼdziko

21 Musalole kuti osautsidwa abwerere mwamanyazi;

22 Dzukani Inu Mulungu ndipo dzitetezeni pa mlandu;

23 Musalekerere phokoso la otsutsana nanu,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado