Salmos 73

NYA

1 Mulungu ndi wabwino ndithu kwa Israeli,

2 Koma kunena za ine, mapazi anga anali pafupi kuterereka;

3 Pakuti ndinkachitira nsanje odzitamandira,

4 Iwo alibe zosautsa;

5 Saona mavuto monga anthu ena;

6 Nʼchifukwa chake kunyada kuli monga mkanda wa mʼkhosi mwawo;

7 Mʼmitima yawo yokhota mumachokera zolakwa;

8 Iwowo amanyogodola ndi kumayankhula zoyipa;

9 Pakamwa pawo pamayankhula monyoza Mulungu kumwamba

10 Nʼchifukwa chake anthu awo amapita kwa iwowo

11 Iwo amati, “Kodi Mulungu angadziwe bwanji?

12 Umu ndi mmene oyipa alili;

13 Ndithudi ine ndawusunga pachabe mtima wanga woyera;

14 Tsiku lonse ndapeza mavuto;

15 Ndikanati, “Ndidzayankhula motere,”

16 Pamene ndinayesa kuti ndimvetse zonsezi,

17 kufikira nditalowa mʼmalo opatulika a Mulungu;

18 Zoonadi Inu munawayika pa malo woterera;

19 Mwamsangamsanga iwo amawonongedwa,

20 Monga loto pamene wina adzuka,

21 Pamene mtima wanga unasautsidwa

22 ndinali wopusa ndi wosadziwa;

23 Komabe ineyo ndili ndi Inu nthawi zonse;

24 Inu mumanditsogolera ndi malangizo anu

25 Kodi kumwamba ndili ndi yani kupatula Inu?

26 Thupi ndi mtima wanga zitha kufowoka,

27 Iwo amene ali kutali ndi Inu adzawonongeka;

28 Koma kunena za Ine ndi kwabwino kukhala pafupi ndi Mulungu.

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado