Salmos 68

NYA

1 Adzuke Mulungu, adani ake amwazikane;

2 Monga momwe mphepo imachotsera utsi; Inu muwawulutsire kutali.

3 Koma olungama asangalale

4 Imbirani Mulungu imbirani dzina lake matamando,

5 Atate wa ana amasiye, mtetezi wa akazi amasiye,

6 Mulungu amakhazikitsa mtima pansi osungulumwa mʼmabanja,

7 Pamene munatuluka kutsogolera anthu anu, Inu Mulungu,

8 dziko lapansi linagwedezeka, miyamba inakhuthula pansi mvula,

9 Munapereka mivumbi yochuluka, Inu Mulungu;

10 Anthu anu anakhala mʼmenemo

11 Ambuye analengeza mawu,

12 “Mafumu ndi ankhondo anathawa mwaliwiro;

13 Ngakhale mukugona pakati pa makola a ziweto,

14 Pamene Wamphamvuzonse anabalalitsa mafumu mʼdziko,

15 Mapiri a Basani ndi mapiri aulemerero;

16 Muyangʼaniranji mwansanje inu mapiri a msonga zambiri,

17 Magaleta a Mulungu ndi osawerengeka,

18 Pamene Inu munakwera mmwamba,

19 Matamando akhale kwa Ambuye, kwa Mulungu Mpulumutsi wathu

20 Mulungu wathu ndi Mulungu amene amapulumutsa;

21 Ndithu Mulungu adzaphwanya mitu ya adani ake,

22 Ambuye akunena kuti, “Ndidzawabweretsa kuchokera ku Basani;

23 Kuti muviyike mapazi anu mʼmagazi a adani anu,

24 Mayendedwe aulemu a anthu anu aonekera poyera, Inu Mulungu;

25 Patsogolo pali oyimba nyimbo pakamwa, pambuyo pawo oyimba nyimbo ndi zipangizo;

26 Tamandani Mulungu mu msonkhano waukulu;

27 Pali fuko lalingʼono la Benjamini, kuwatsogolera,

28 Kungani mphamvu zanu Mulungu;

29 Chifukwa cha Nyumba yanu ku Yerusalemu,

30 Dzudzulani chirombo pakati pa mabango,

31 Nthumwi zidzachokera ku Igupto;

32 Imbirani Mulungu Inu mafumu a dziko lapansi

33 Kwa Iye amene amakwera pa mitambo yakalekale ya mmwamba

34 Lengezani za mphamvu za Mulungu,

35 Ndinu woopsa, Inu Mulungu mʼmalo anu opatulika;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado