Salmos 67

NYA

1 Yehova atikomere mtima ndi kutidalitsa,

2 Kuti njira zanu zidziwike pa dziko lapansi,

3 Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu;

4 Mitundu yonse ya anthu isangalale ndi kuyimba mwachimwemwe,

5 Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu;

6 Nthaka yabereka zokolola zake;

7 Mulungu atidalitse

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado