1 Yehova atikomere mtima ndi kutidalitsa,
2 Kuti njira zanu zidziwike pa dziko lapansi,
3 Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu;
4 Mitundu yonse ya anthu isangalale ndi kuyimba mwachimwemwe,
5 Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu;
6 Nthaka yabereka zokolola zake;
7 Mulungu atidalitse