Salmos 66

NYA

1 Fuwulani kwa Mulungu ndi chimwemwe, dziko lonse lapansi!

2 Imbani ulemerero wa dzina lake;

3 Nenani kwa Mulungu, “Ntchito zanu ndi zoopsa ndithu!

4 Dziko lonse lapansi limaweramira inu;

5 Bwerani mudzaone zimene Mulungu wachita,

6 Iye anasandutsa nyanja kukhala malo owuma,

7 Iye amalamulira ndi mphamvu zake mpaka muyaya,

8 Tamandani Mulungu wathu, inu mitundu ya anthu,

9 Iye watchinjiriza miyoyo yathu

10 Pakuti Inu Mulungu munatiyesa;

11 Inu mwatilowetsa mʼndende

12 Inu munalola kuti anthu akwere pa mitu yathu;

13 Ine ndidzabwera ku Nyumba yanu ndi nsembe zopsereza

14 Malumbiro amene milomo yanga inalonjeza

15 Ndidzapereka nsembe nyama zonenepa kwa Inu

16 Bwerani ndipo mudzamve inu nonse amene mumaopa Mulungu.

17 Ndinafuwula kwa Iye ndi pakamwa panga,

18 Ndikanasekerera tchimo mu mtima mwanga

19 koma ndithu Mulungu wamvetsera

20 Matamando akhale kwa Mulungu

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado