Salmos 65

NYA

1 Matamando akudikira Inu Mulungu mu Ziyoni;

2 Inu amene mumamva pemphero,

3 Pamene tinathedwa nzeru ndi machimo,

4 Odala iwo amene inu muwasankha

5 Mumatiyankha ife ndi ntchito zodabwitsa zachilungamo,

6 amene munapanga mapiri ndi mphamvu zanu,

7 Amene munakhalitsa bata nyanja

8 Iwo amene akukhala kutali amaopa zizindikiro zozizwitsa zanu;

9 Inu mumasamalira dziko lapansi ndi kulithirira;

10 Mwadzaza nthaka yake ndi madzi ndi kusalaza migula yake,

11 Inu mumaveka chaka ndi zinthu zochuluka,

12 Malo a udzu a mʼchipululu amasefukira;

13 Madambo akutidwa ndi zoweta

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado