1 Matamando akudikira Inu Mulungu mu Ziyoni;
2 Inu amene mumamva pemphero,
3 Pamene tinathedwa nzeru ndi machimo,
4 Odala iwo amene inu muwasankha
5 Mumatiyankha ife ndi ntchito zodabwitsa zachilungamo,
6 amene munapanga mapiri ndi mphamvu zanu,
7 Amene munakhalitsa bata nyanja
8 Iwo amene akukhala kutali amaopa zizindikiro zozizwitsa zanu;
9 Inu mumasamalira dziko lapansi ndi kulithirira;
10 Mwadzaza nthaka yake ndi madzi ndi kusalaza migula yake,
11 Inu mumaveka chaka ndi zinthu zochuluka,
12 Malo a udzu a mʼchipululu amasefukira;
13 Madambo akutidwa ndi zoweta