1 Ndimvereni Mulungu pomwe ndikunena madandawulo anga;
2 Ndibiseni ku chiwembu cha anthu oyipa,
3 Iwo amanola malilime awo ngati malupanga,
4 Iwo amaponya mivi yawo ali pa malo wobisala kwa munthu wosalakwa;
5 Iwo amalimbikitsana wina ndi mnzake pa chikonzero chawo choyipa,
6 Iwo amakonzekera zosalungama ndipo amati,
7 Koma Mulungu adzawalasa ndi mivi;
8 Iye adzatembenuza milomo yawoyo kuwatsutsa
9 Anthu onse adzachita mantha;
10 Lolani wolungama akondwere mwa Yehova