1 Inu Mulungu, ndinu Mulungu wanga,
2 Inu ndinakuonani ku malo anu opatulika
3 Chifukwa chikondi chanu
4 Ndidzakutamandani masiku onse a moyo wanga,
5 Mudzakhutitsa moyo wanga ndi zonona.
6 Pa bedi panga ndimakumbukira inu;
7 Chifukwa ndinu thandizo langa,
8 Moyo wanga umakangamira Inu;
9 Iwo amene akufunafuna moyo wanga adzawonongedwa;
10 Iwo adzaperekedwa ku lupanga
11 Koma mfumu idzakondwera mwa Mulungu;