Salmos 63

NYA

1 Inu Mulungu, ndinu Mulungu wanga,

2 Inu ndinakuonani ku malo anu opatulika

3 Chifukwa chikondi chanu

4 Ndidzakutamandani masiku onse a moyo wanga,

5 Mudzakhutitsa moyo wanga ndi zonona.

6 Pa bedi panga ndimakumbukira inu;

7 Chifukwa ndinu thandizo langa,

8 Moyo wanga umakangamira Inu;

9 Iwo amene akufunafuna moyo wanga adzawonongedwa;

10 Iwo adzaperekedwa ku lupanga

11 Koma mfumu idzakondwera mwa Mulungu;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado