1 Moyo wanga umapeza mpumulo mwa Mulungu yekha;
2 Iye yekhayo ndiye thanthwe langa ndi chipulumutso changa;
3 Kodi nonsenu mudzalimbana naye munthu mpaka liti?
4 Iwo akufunitsitsa kumugwetsa
5 Peza mpumulo mwa Mulungu yekhayo iwe moyo wanga;
6 Iye yekhayo ndiye thanthwe langa ndi chipulumutso changa;
7 Chipulumutso changa ndi ulemu wanga zimachokera kwa Mulungu:
8 Dalirani Iye nthawi zonse, inu anthu;
9 Anthu wamba ndi mpweya chabe;
10 Musadalire kulanda mwachinyengo
11 Mulungu wayankhula kamodzi,
12 komanso Inu Ambuye, chikondi chanu nʼchosasinthika.