Salmos 62

NYA

1 Moyo wanga umapeza mpumulo mwa Mulungu yekha;

2 Iye yekhayo ndiye thanthwe langa ndi chipulumutso changa;

3 Kodi nonsenu mudzalimbana naye munthu mpaka liti?

4 Iwo akufunitsitsa kumugwetsa

5 Peza mpumulo mwa Mulungu yekhayo iwe moyo wanga;

6 Iye yekhayo ndiye thanthwe langa ndi chipulumutso changa;

7 Chipulumutso changa ndi ulemu wanga zimachokera kwa Mulungu:

8 Dalirani Iye nthawi zonse, inu anthu;

9 Anthu wamba ndi mpweya chabe;

10 Musadalire kulanda mwachinyengo

11 Mulungu wayankhula kamodzi,

12 komanso Inu Ambuye, chikondi chanu nʼchosasinthika.

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado