1 Imvani kulira kwanga, Inu Mulungu;
2 Kuchokera ku malekezero a dziko lapansi ine ndimayitana Inu
3 Pakuti Inu mwakhala pothawirapo panga,
4 Ine ndikulakalaka kukhala mʼtenti yanu kwamuyaya
5 Pakuti Inu Mulungu mwamva malumbiro anga;
6 Wonjezerani masiku a moyo wa mfumu,
7 Iye akhale pa mpando waufumu pamaso pa Mulungu kwamuyaya;
8 Kotero ndidzayimba matamando kwamuyaya pa dzina lanu