Salmos 61

NYA

1 Imvani kulira kwanga, Inu Mulungu;

2 Kuchokera ku malekezero a dziko lapansi ine ndimayitana Inu

3 Pakuti Inu mwakhala pothawirapo panga,

4 Ine ndikulakalaka kukhala mʼtenti yanu kwamuyaya

5 Pakuti Inu Mulungu mwamva malumbiro anga;

6 Wonjezerani masiku a moyo wa mfumu,

7 Iye akhale pa mpando waufumu pamaso pa Mulungu kwamuyaya;

8 Kotero ndidzayimba matamando kwamuyaya pa dzina lanu

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado