1 Inu Mulungu mwatikanatu ife, ndipo mwatiwonongera otiteteza.
2 Inu mwagwedeza dziko ndipo mwalingʼamba,
3 Inu mwaonetsa anthu anu nthawi za mavuto;
4 Koma kwa iwo amene amaopa Inu, Inu mwakweza mbendera
5 Tipulumutseni ndi kutithandiza ndi dzanja lanu lamanja,
6 Mulungu wayankhula kuchokera ku malo ake opatulika:
7 Giliyadi ndi wanga, Manase ndi wanganso;
8 Mowabu ndi mbale yanga yosambira,
9 Adzandifikitse ndani ku mzinda wotetezedwa?
10 Kodi si Inu Mulungu, Inu amene mwatikana ife
11 Tipatseni chithandizo kuti tilimbane ndi mdani wathu,
12 Chifukwa cha Mulungu, ife tidzapeza chipambano